1.a.Kodi mayina awa adachokera ku chiyankhulo chanji?(malikisi 4)
1.b kodi afotokozi ali m`munsiwa adapangidwa bwanji? (maliki 6)
2.a.Pangani ziganizo ndi nthawi za aneni zotsatirazi: (malikisi 6)
2.b.Tchulani mitundu ya agwirizanitsi omwe ali ndi mzere kunsi kwake mu ziganizo zotsatirazi (malikisi 4)
3.a. Lembani ziganizo zosonyeza ntchito za ‘ti’ zotsatirazi ndipo mutseke mzere kunsi kwake (malikisi 6)
Tchulani ntchito za akapandamneni omwe atsekedwa mzere kunsi kwawo mziganizo zotsatirazi. (malikisi 4)
4.Phwanyani chiganizo chotsatirachi pounika mawu aliwonse pawokhapawokha